28/03/2026
'Nginde' settles for 3-5-2 against Dedza Dynamos:
🔵Mtete to man the sticks
🔵 New signings Kambirinya, Nahipa and Mithi make the grade
Ekhaya Farms Foods Kasupe Water Smile Life Insurance Company Limited
28/03/2026
Kuli kuthizimulana lero malawi ndi Zambia
28/03/2026
Zayambika lero
Apwetekana.
27/03/2026
Mwimiliri wakumphala ya malango muchigawa cha mangochi MonkeyBay Gerald Kazembe walomba Boma kwizira ku unduna wakuona vya milimo kuti lighanaghanire za kukwezga malipiro ku wanthu wakugwira ntchito zapa nyumba ngati kulera wana na kuphika.
Mazgu ghawo wandula kuti malipiro ghakwenera kuyambira pa k200,000.
Ba Kazembe wayooya mazgu agha mu mphala ya malango pakuwikapo maghano ghano ghawo ku unduna wakuona vya milimo pakukhwaskana na wanthu wakugwira ntchito zapa nyumba.
(Christopher Benjamin Chiwaka 27/03/26)
27/03/2026
Zipani zikupitilira kuzuzula Boma posalemekedza kapena kudzuza wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino Dr Jane Ansah.
Patangodusa masiku ochepa Chipani cha UTM chitadzuzula mchitidwe umenewu nachoso Chipani cha UDF chabwera poyera kuyankhulapo pa nkhaza zimenezi.
Malinga ndi chikalata chomwe Yabenura Broadcasting Station YBS yaona chati zimenezi sizoyenera chifukwa wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko amasankhidwa ndi a malawi kudzera pa vote.
Wolemba Christopher Benjamin Chiwaka
27/03/2026
26/03/2026
Ekhaya FC have completed the signing of 22-year-old midfielder Isaiah Nyirenda from Mzuzu City Hammers, with the player putting pen to paper on a three-year deal.
26/03/2026
FAM president Fleetwood Haiya has encouraged the Flames to stay committed as they travel to Francistown for the Mukuru Four Nations Tournament, urging them to build on their recent performance and calling on Malawians to support the team.
Mlongozgi wa wupu wa Farm walimbikiska wazgalili wa timu ya chalo chino kuti wakalimbikire mwakuti wena Malawi wayambeso kuyitemwa timu iyi. Haiya wandula makani agha apo walayirananga na timu iyi apo yanyamkanga kuluta ku Boswana kukatora nawo lwande mchiphalizgano cha Mkuru 4 nations pa chingelezi .
26/03/2026
Timu ya zgalo za bola la malundi ya Ekhaya FC yaphalazga za mzgalili mupsa ku timu iyi Chimwemwe Chunga uyo wafumira ku timu ya Mzuzu City Hummers ndipo wasayinira kukhala ku Ekhaya FC kwa vilimika vitatu.
Chimwemwe Chunga ngwa kuzgalira pakati.
Wakulemba ndine Blessings Joshua Ndhlozi
27/03/2026
17/03/2026
Ba Moir Walita Mkandawire awo wakuyimira Chipani chakulamula Boma cha Democratic Progressive Party waponya voti yawo pa sukulu ya St Denis apo wakalembeskera.
Wakulemba Christopher Benjamin Chiwaka
17/03/2026
17/03/2026
Wachiwiri wina kwa mtsogoleri wadziko lino Enock Kamzingeni Chihana aponya voti yawo yosankha Phungu wa nyumba ya malamuro.
Ndipo iwo alimbikitsa anthu kuti aponye voti mwa bata ndi mtendere.
Christopher Benjamin Chiwaka
17/03/2026