Koma Bawo osaiwalatu kaamba ka holiday imeneyi
Bawo Pa Malawi
Kulemekeza chikhalidwe kuyambile pa chidwi chathu pamasewero a Bawo.
Mwadzuka Bwanji A Malawi.
15/07/2023
Iyi ndi Kameza Round-About Bawo Club. Akufuna aipange challenge ndindani tikaone katakwe kunkhani yotakata .
Mwadzuka bwanji a Malawi. Kwazizilatu, yemwe akufuna bawo tiyakhulane.
Ngati mukufuna kudziwa zambili zokhuzana ndi masewero a Bawo komanso omwe amayendesa masewelowa muno Malawi. Chonde Yankhulanani ndi awa;
Chairman Mr Banda: +265 992 50 14 06
Vice Chair Mr Alick: +265 993 63 31 12
Secretary Mr Frank:
+265 888 57 35 70
NTHAWI YAKWANA. AKATSWILI ODZIWA BAWO ADZIWIKE PANO PA MALAWI.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Location
Category
Website
Address
Blantyre