14/07/2025
#
Ilyas Abdul Karim, phungu wadera la kumwera kwa boma la Chikwawa waulura kuti ayima payekha pachisankho chikudzachi.
Iye anali wa chipani cha Malawi Congress MCP.
Ndipo waulura izi lero pa Ngabu pomwe Pali mafumu ndi anthu osiyananasiyana
22/02/2024
Osewera atatu lanjes nkhoma maxwell gasten phodo goalkeeper Christopher mikuwa wa mafco ndi omwe akhare akulimbilina mphondo ya osewera omwe asewera bwino airtel top 8 season ya 2023 nkhoma ngat top goal score komanso phodo ngat puliya amene wasewera magemu awiri ndikugolesa zigoli ziwili pamene Christopher mikuwa ngat otchinga pagolo wapamwamba