31/08/2026
Confederation of African Football (CAF), yasankha oyimbira asanu kuti akayimbire masewero a mpikisano wa Champions League komanso Confederations Cup.
Easter Zimba ndi amene adzaimbire masewero a Confederation Cup pakati pa Unam FC ya ku Namibia ndi Kabuscorp de Palanca ya m'dziko la Angola pa bwalo la Luanda Estadio 11 de Novembro pa 5 September 2026.
Samuel Fudzulani ndi Lameck Phiri asankhidwa kuti akagwire ntchito ngati othandizira pamene David Chinoko ndi amene akakhale oyimbira wapadera.
Chinoko wapatsidwanso masewero a Champions League pakati pa Foresters FC ya ku Seychelles ndi Willete de Benguela omwe adzaseweredwe pa 10 September 2026 pa bwalo la Lubango-Estadio Nacional da Tundavala.
Fudzulani komanso Sibusiso Sibande ndi amene adzagwire ntchito ngati othandizira patsikuli, pamene Zimba ndiamene adzakhale bwana wa oyimbirawa.
Mkulu wa oyimbira ku Football Association of Malawi (FAM), Duncan Lengani, wati ndiokondwa ndi chiwerengerochi zomwe zikuonetsa mpira ukupita patsogolo.
31/08/2026
The five highest-paid footballers on the African continent are all playing in Libya.
1. Fiston Mayele ๐จ๐ฉ | $5 million | Al Ahli Tripoli
2. Kwasi Sibo ๐ฌ๐ญ | $5 million | Al-Swehly
3. Mohamed Tougai ๐ฉ๐ฟ | $3.7 million | Al Ahli Tripoli
4. Jean Claude Girumugisha ๐ง๐ฎ | $2.4 million | Al Ahli Tripoli
5. Lameck Banda ๐ฟ๐ฒ | $1.85 million | Al-Swehly
31/08/2026
Bungwe la FAM lalengeza kuti masewero a ndime yotsiriza ya chikho cha Airtel Top 8, pakati pa Mighty Wanderers ndi Ekhaya FC, atulutsa ndalama zokwana K87.3 million.
Masewerowa anachitikira pa Bingu National Stadium ku Lilongwe la mulungu, pa 30 August, ndipo Ekhaya FC inagonjetsa Wanderers 2-1 kuti ikhale katswiri watsopano wa chikhochi.
Mkulu owona za malonda ku bungwe la FAM, Mayamiko Kafwamba, watiuza kuti, pa ndalamazi, ma timu a Wanderers ndi Ekhaya atenga K12.6 million timu iliyonse.
Malinga ndi a Kafwamba, ndondomeko yogulitsa ma tikiti pa tsiku la mpira lomwelo inathandiza chifukwa kunalibe ma tikiti a chinyengo.
Koma a Kafwamba ati mchitidwe wa anthu ena ochepa, olowa m'bwaloli modumpha mpanda kapenanso kubowola wire, amene anazungulira bwaloli, unachitika.
Iwo ati bungwe la FAM lipitiriza kukambirana ndi nthambi zokhudzidwa, kuphatikizapo a chitetezo, pofuna njira zothetseratu vutoli pamene timu ya Flames idzikonzekera kusewera ndi South Sudan mu Africa Cup of Nations mwezi wa September.
31/08/2026
FAM YASANKHA BOB MPINGAJIRA KUKHALA MPHUZITSI WA FLAMES U-23
Pasanathe maola 24 timu ya Mighty Wanderers FC itaimitsa ntchito a Bob Mpinganjira, bungwe la Football Association of Malawi (FAM) lamusankha kukhala mphunzitsi watimu ya dziko lino ya osewera osapitilira zaka 23.
Pakadali pano, timuyi ikuyembekezeka kukumana ndi Eswatini mu gawo loyamba la masewero ozipezera malo ku mpikisano wa U-23 Africa Cup of Nations.
Masewerowa akuyembekezeka kuchitika pa 28 September 2026.
31/08/2026
Mighty Wanderers FC have suspended head coach Bob Mpinganjira with immediate effect following a string of inconsistent performances, including their defeat to Ekhaya FC in the Airtel Top 8 final.
The Nomads announced the decision in a statement signed by Board Secretary Chancy Gondwe on behalf of the Board of Directors, without giving specific reasons for the suspension.
The club said it will appoint an interim head coach within the next 48 hours as it moves to restructure the technical panel.
30/08/2026
Timu ya Ekhaya ndi akatswiri achikho cha Airtel Top 8 Zamadolo atagonjetsa timu ya Mighty Wanderers 2-1 bwalo la Bingu Ku Lilongwe.
Ekhaya inapeza zigoli zake kudzera kwa Blessings Malinda komanso Allen Chihana pomwe Wanderers inagoletsa kudzera mwa Mphatso Kamanga.
Timu ya Ekhaya yatenga ukatswiriwu pamene kanali koyamba kusewera nawo mu mpikisano wa Airtel Top 8 Zamadolo.
25/08/2026
Msika wogula ndi kugulitsa osewera watsegulidwa lero.
Bungwe loyendetsa masewero a mpira wamiyendo la Fam lalengeza izi kudzera patsamba la mchezo.
Malinga ndi bungweli msikawu udzatsekedwa pa 21 September.
Izi zikutanthauza kuti matimu ali ndi ufulu wogula kapena kugulitsa osewera pakadali pano.
Pakadali pano katswiri wa Blue Eagles Fahad Mcheka komanso Rashid Dah wa Luanar Mitundu ndi ena mwa osewera omwe akufunidwa kwambiri.
25/08/2026
FCB Nyasa Big Bullets have signed a 26-year-old Liberian, Sheku Sheriff, from LPRC Oilers on a two-year deal
Maule mwamulandira bwanji katundu ?
21/08/2026
๐จ ๐๐
๐
๐๐๐๐๐: Premier League has confirmed ๐ง๐๐ฐ ๐ซ๐ฎ๐ฅ๐๐ฌ for the 2026/27 season. ๐๐ด๓ ง๓ ข๓ ฅ๓ ฎ๓ ง๓ ฟ
โ
๐๐๐ฐ ๐ซ๐ฎ๐ฅ๐๐ฌ ๐๐๐ข๐ง๐ ๐ข๐ง๐ญ๐ซ๐จ๐๐ฎ๐๐๐:
โฆฟ Injured players must now stay off the pitch for at least ๐ ๐ฆ๐ข๐ง๐ฎ๐ญ๐, up from 30 seconds
โฆฟ A ๐-๐ฌ๐๐๐จ๐ง๐ ๐๐จ๐ฎ๐ง๐ญ๐๐จ๐ฐ๐ง for throw-ins and goal-kicks, with the restart reversed if delayed
โฆฟ Substituted players have just ๐๐ ๐ฌ๐๐๐จ๐ง๐๐ฌ to leave the field, or their replacement waits until the next stoppage
โฆฟ A new VAR review specifically for clearly ๐ฐ๐ซ๐จ๐ง๐ ๐ฌ๐๐๐จ๐ง๐ ๐ฒ๐๐ฅ๐ฅ๐จ๐ฐ cards resulting in a red
โฆฟ A trial requiring managers to nominate an outfield player to leave the pitch for a minute whenever play is stopped for a goalkeeper injury
โ Whatโs ๐ง๐จ๐ญ ๐๐จ๐ฆ๐ข๐ง๐ from this summerโs World Cup:
โฆฟ Hydration breaks
โฆฟ VAR reviews for incorrectly awarded corners
โฆฟ The red-card protocol for players covering their mouths
โฆฟ Yellow cards being reversed for mistaken identity or diving, VAR can only correct who was booked, not the decision itself
๐๐ ๐๐๐ ๐๐๐๐๐ ๐๐๐๐ ๐๐๐ ๐๐๐๐๐๐๐?